Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 50:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo Farao anati, Pita, kaike atate wako, monga iye anakulumbiritsa iwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo Farao anati, Pita, kaike atate wako, monga iye anakulumbiritsa iwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Farao adamuyankha kuti, “Pita ukaike atate ako monga momwe adakulumbiritsira.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Farao anati, “Pita ukayike abambo ako monga anakulumbiritsa kuti uchite.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 50:6
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Israele anati kwa Yosefe, Taona, ndilinkufa ine; Mulungu adzakhala ndi iwe, adzakubwezanso iwe ku dziko la makolo ako.


Atate wanga anandilumbiritsa ine, kuti, Taona, ndilinkufa; m'manda m'mene ndadzikonzeratu ndekha m'dziko la Kanani, m'menemo udzandiika ine. Tsopano mundiloletu, ndikwereko, ndipite, ndikaike atate wanga, nditatero ndidzabweranso.


Ndipo Yosefe anapita kukaika atate wake; ndipo anakwera pamodzi ndi akapolo onse a Farao, ndi akulu a pa mbumba yake, ndi akulu onse a m'dziko la Ejipito,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa