Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 50:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo Yosefe anapita kukaika atate wake; ndipo anakwera pamodzi ndi akapolo onse a Farao, ndi akulu a pa mbumba yake, ndi akulu onse a m'dziko la Ejipito,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo Yosefe anapita kukaika atate wake; ndipo anakwera pamodzi ndi akapolo onse a Farao, ndi akulu a pa mbumba yake, ndi akulu onse a m'dziko la Ejipito,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Yosefe adapita kukaika bambo wake. Ndipo nduna zonse za Farao, akuluakulu a bwalo, ndi anthu ena otchuka a ku Ejipito adamperekeza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Kotero Yosefe anapita kukayika abambo ake. Nduna zonse za Farao, akuluakulu a bwalo lake ndi akuluakulu a ku Igupto, anapita naye pamodzi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 50:7
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anabwera nacho chuma chonse, nabwera naye Loti yemwe ndi chuma chake, ndi akazi ndi anthu omwe.


Ndipo Farao anati, Pita, kaike atate wako, monga iye anakulumbiritsa iwe.


ndi mbumba yonse ya Yosefe ndi abale ake, ndi mbumba ya atate wake: ang'ono ao okha, ndi nkhosa zao, ndi ng'ombe zao, anazisiya m'dziko la Goseni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa