Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 50:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo ataika atate wake, Yosefe anabwera ku Ejipito, iye ndi abale ake, ndi onse amene anakwera pamodzi naye kukaika atate wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo ataika atate wake, Yosefe anabwera ku Ejipito, iye ndi abale ake, ndi onse amene anakwera pamodzi naye kukaika atate wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Yosefe ataika bambo wake m'manda, adabwerera ku Ejipito ndi abale ake aja, pamodzi ndi onse amene adamperekeza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Atatha kuyika abambo ake, Yosefe anabwerera ku Igupto, pamodzi ndi abale ake ndi onse amene anapita nawo kukayika abambo ake.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 50:14
2 Mawu Ofanana  

chifukwa kuti ana ake aamuna anamnyamula iye kulowa naye m'dziko la Kanani, ndi kumuika iye m'phanga la munda wa Makipela, limene Abrahamu analigula pamodzi ndi munda, likhale poikira pake, kwa Efuroni Muhiti, patsogolo pa Mamure.


Ndipo pamene abale ake a Yosefe anaona kuti atate wao anafa, anati, Kapena Yosefe adzatida ife, ndipo adzatibwezera ife zoipa zonse tidamchitira iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa