Genesis 50:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo ana ake aamuna anamchitira iye monga anawalamulira iwo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo ana ake amuna anamchitira iye monga anawalamulira iwo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ana a Yakobe adachitadi monga momwe bambo wao adaaŵalamulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Choncho ana a Yakobo anachita monga momwe abambo awo anawalamula: Onani mutuwo |