Genesis 50:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Yosefe anagwa pa nkhope ya atate wake, namlirira iye nampsompsona iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Yosefe anagwa pa nkhope ya atate wake, namlirira iye nampsompsona iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pomwepo Yosefe adadzigwetsa pa mtembo wa bambo wake akulira, kwinaku akumpsompsona bambo wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Kenaka Yosefe anadzigwetsa pa nkhope ya abambo ake, nawapsompsona kwinaku akulira. Onani mutuwo |