Genesis 49:33 - Buku Lopatulika33 Pamene Yakobo anatha kulangiza ana ake aamuna, anafunya mapazi ake pakama, natsirizika, nasonkhanitsidwa kwa anthu a mtundu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Pamene Yakobo anatha kulangiza ana ake amuna, anafunya mapazi ake pakama, natsirizika, nasonkhanizidwa kwa anthu a mtundu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Tsono Yakobe atamaliza kulangiza ana ake, adabwezeranso mapazi ake m'bedi ndipo adamwalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Yakobo atamaliza kupereka malangizo kwa ana ake, anabwezera miyendo yake pa bedi, namwalira ndipo anakakhala ndi anthu a mtundu wake. Onani mutuwo |