Genesis 5:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Adamu anakhala ndi moyo zaka zana limodzi kudza makumi atatu, nabala mwana wamwamuna m'chifanizo chake; namutcha dzina lake Seti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Adamu anakhala ndi moyo zaka zana limodzi kudza makumi atatu, nabala mwana wamwamuna m'chifanizo chake; namutcha dzina lake Seti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Adamu ali wa zaka 130 adabereka mwana wofanafana ndi iye, namutcha Seti. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamene Adamu anali ndi zaka 130, anabereka mwana wamwamuna wofanana naye ndipo anamutcha Seti. Onani mutuwo |