Genesis 5:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamene Adamu anali ndi zaka 130, anabereka mwana wamwamuna wofanana naye ndipo anamutcha Seti. Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Ndipo Adamu anakhala ndi moyo zaka zana limodzi kudza makumi atatu, nabala mwana wamwamuna m'chifanizo chake; namutcha dzina lake Seti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Adamu anakhala ndi moyo zaka zana limodzi kudza makumi atatu, nabala mwana wamwamuna m'chifanizo chake; namutcha dzina lake Seti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Adamu ali wa zaka 130 adabereka mwana wofanafana ndi iye, namutcha Seti. Onani mutuwo |