Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 5:20 - Buku Lopatulika

20 masiku ake onse a Yaredi anali zaka mazana asanu ndi anai kudza makumi asanu ndi limodzi ndi ziwiri: ndipo anamwalira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 masiku ake onse a Yaredi anali zaka mazana asanu ndi anai kudza makumi asanu ndi limodzi ndi ziwiri: ndipo anamwalira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Adamwalira ali wa zaka 962.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Zaka zonse za Yaredi zinali 962 ndipo anamwalira.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 5:20
3 Mawu Ofanana  

ndipo Yaredi anakhala ndi moyo, atabala Enoki, zaka mazana asanu ndi atatu, nabala ana aamuna ndi aakazi;


Ndipo Enoki anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi limodzi kudza zisanu, nabala Metusela:


Ndipo masiku onse a Nowa anali mazana asanu ndi anai kudza makumi asanu: ndipo anamwalira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa