Genesis 5:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo Yaredi anakhala ndi moyo zaka zana kudza makumi asanu ndi limodzi ndi ziwiri, nabala Enoki; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo Yaredi anakhala ndi moyo zaka zana kudza makumi asanu ndi limodzi ndi ziwiri, nabala Enoki; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Yaredi ali wa zaka 162, adabereka mwana dzina lake Enoki, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pamene Yaredi anali ndi zaka 162, anabereka Enoki. Onani mutuwo |