Genesis 49:9 - Buku Lopatulika9 Yuda ndi mwana wa mkango, kuchokera kuzomotola, mwananga, wakwera; anawerama pansi, anabwatama ngati mkango, ndipo ngati mkango waukazi; ndani adzamukitsa iye? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Yuda ndi mwana wa mkango, kuchokera kuzomotola, mwananga, wakwera; anawerama pansi, anabwatama ngati mkango, ndipo ngati mkango waukazi; ndani adzamukitsa iye? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Yuda ali ngati msona wa mkango. Ukapha, umabwereranso kumalo kumene umabisala. Yuda ali ngati mkango, amatambasuka nagona pansi. Iye ndi mkangodi, ndipo palibe amene angalimbe mtima kuti amdzutse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Yuda ali ngati mwana wa mkango; umabwerera ku malo ako ndi zofunkha, mwana wanga. Monga mkango, amadziwongola ndi kugona pansi, ndipo ngati mkango waukazi, ndani angalimbe mtima kumudzutsa? Onani mutuwo |