Genesis 49:10 - Buku Lopatulika10 Ndodo yachifumu siidzachoka mwa Yuda, kapena wolamulira pakati pa mapazi ake, kufikira atadza Silo; ndipo anthu adzamvera iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndodo yachifumu siidzachoka mwa Yuda, kapena wolamulira pakati pa mapazi ake, kufikira atadza Silo; ndipo anthu adzamvera iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndodo yaufumu siidzachoka mwa Yuda, adzachita kuupanira ufumu umenewo, adzasunga mphamvu zake, mpaka mwiniwake weniweni atabwera, wodzalamulira anthu onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndodo yaufumu sidzachoka mwa Yuda, udzawupanirira ulamuliro motero kuti palibe amene adzawuchotse, mpaka mwini wake weniweni atabwera ndipo mitundu yonse ya anthu idzamumvera. Onani mutuwo |