Genesis 49:11 - Buku Lopatulika11 Adamanga mwana wa kavalo wake pampesa, ndi mwana wa bulu wake pa mpesa wosankhika; natsuka malaya ake m'vinyo, ndi chofunda chake m'mwazi wa mphesa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Adamanga mwana wa kavalo wake pampesa, ndi mwana wa bulu wake pa mpesa wosankhika; natsuka malaya ake m'vinyo, ndi chofunda chake m'mwazi wa mphesa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Bulu wake amamumangirira ku mtengo wamphesa, mwanawabulu ku mpesa wabwino. Zovala zake amazichapa mu vinyo, mu vinyo wofiira ngati magazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndiye amene amamangirira bulu wake wamkazi kumtengo wa mpesa, ndi mwana wa bulu ku nthambi ya mpesa wabwino. Ndi iye amene amachapa zovala zake mu vinyo; ndi mkanjo wake mu vinyo wofiira ngati magazi. Onani mutuwo |