Genesis 49:27 - Buku Lopatulika27 Benjamini ndiye mmbulu wakulusalusa; m'mamawa adzadya chomotola, madzulo adzagawa zofunkha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Benjamini ndiye mmbulu wakulusalusa; m'mamawa adzadya chomotola, madzulo adzagawa zofunkha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 “Benjamini ali ngati mmbulu wolusa umene m'maŵa umapha ndi kudya zimene udagwira, ndipo madzulo umagaŵa zimene udagwirazo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 “Benjamini ali ngati mʼmbulu wolusa; umene mmawa umapha ndi kudya zofunkha, ndipo madzulo umagawa zofunkhazo,” Onani mutuwo |