Genesis 49:26 - Buku Lopatulika26 Madalitso a atate wako apambana mphamvu ndi madalitso a makolo anga, kufikira ku malekezero a patali a mapiri a chikhalire. Adzakhala pamutu wa Yosefe, ndi pakati pamutu wa iye amene ali wolekanitsidwa ndi abale ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Madalitso a atate wako apambana mphamvu ndi madalitso a makolo anga, aufikira ku malekezero a patali a mapiri a chikhalire. Adzakhala pa mutu wa Yosefe, ndi pakati pa mutu wa iye amene ali wolekanitsidwa ndi abale ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Madalitso a bambo wako ndi amphamvu kupambana madalitso a mapiri amuyaya, kupambananso zabwino za ku zitunda zamuyaya. Zimenezi zidzakhala pamutu pa Yosefe, pamphumi pa kalonga amene adampatula pakati pa abale ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Madalitso a kholo lako ndi amphamvu kuposa madalitso a mapiri akale oposa zabwino za ku zitunda zamgonagona. Zonse izi zikhale pamutu pa Yosefe, pa mphumi pa wopatulika uja amene anapatulidwa pakati pa abale ake. Onani mutuwo |