Genesis 49:22 - Buku Lopatulika22 Yosefe ndi nthambi yobala, nthambi yobala pambali pa kasupe; nthambi zake ziyangayanga palinga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Yosefe ndi nthambi yobala, nthambi yobala pambali pa kasupe; nthambi zake ziyangayanga palinga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 “Yosefe ali ngati nthambi yobala zipatso, nthambi yobala zipatso pafupi ndi kasupe, nthambi yotambasuka pa khoma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 “Yosefe ali ngati mtengo wobereka zipatso, mtengo wobereka zipatso pafupi ndi kasupe, nthambi zake zimayanga pa chipupa cha mwala. Onani mutuwo |