Genesis 49:23 - Buku Lopatulika23 Eni uta anavutitsa iye kwambiri, namponyera iye, namzunza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Eni uta anavutitsa iye kwambiri, namponyera iye, namzunza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Adani ake adalimbana naye mwankhalwe, namthamangitsa ndi mauta ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Alenje a uta anamuchita chiwembu mwankhanza; anamuthamangitsa ndi mauta awo. Onani mutuwo |