Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 49:17 - Buku Lopatulika

17 Dani adzakhala njoka m'khwalala, songo panjira, imene iluma zitendene za kavalo, kuti womkwera wake agwe chambuyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Dani adzakhala njoka m'khwalala, songo panjira, imene iluma zitende za kavalo, kuti womkwera wake agwe chambuyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Dani adzakhala ngati njoka pambali pa mseu, njoka yaululu ndithu m'mbali mwa njira, yoluma ku chidendene cha kavalo, kotero kuti wokwerapo wake adzagwa chagada.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Dani adzakhala ngati njoka ya mʼmphepete mwa msewu, songo yokhala mʼnjira imene imaluma chidendene cha kavalo kuti wokwerapoyo agwe chagada.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 49:17
8 Mawu Ofanana  

Dani adzaweruza anthu ake, monga limodzi la mafuko a Israele.


Ndadikira chipulumutso chanu, Yehova.


Ndi a Adani akupangira nkhondo zikwi makumi awiri mphambu zisanu ndi zitatu kudza mazana asanu ndi limodzi.


Pa chitsiriziro chake aluma ngati njoka, najompha ngati mamba.


Njoka ikaluma isanalodzedwe, watsenga saona mphotho.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa