Genesis 49:16 - Buku Lopatulika16 Dani adzaweruza anthu ake, monga limodzi la mafuko a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Dani adzaweruza anthu ake, monga limodzi la mafuko a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 “Dani adzalamulira anthu ake. Anthuwo adzalingana ndi mafuko ena a Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 “Dani adzaweruza mwachilungamo anthu ake monga limodzi mwa mafuko a anthu a mu Israeli. Onani mutuwo |