Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 49:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo anaona popumulapo kuti panali pabwino, ndi dziko kuti linali lokondweretsa; ndipo anaweramitsa phewa lake kuti anyamule, nakhala kapolo wakugwira ntchito ya msonkho.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo anaona popumulapo kuti panali pabwino, ndi dziko kuti linali lokondweretsa; ndipo anaweramitsa phewa lake kuti anyamule, nakhala kapolo wakugwira ntchito ya msonkho.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Ataona kukoma kwa malo ousirapowo, ndi kukongola kwa dzikolo. Adaŵeramitsa msana kuti anyamule katundu wake, ndipo adasanduka womagwira ntchito yaukapolo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Ataona ubwino wake wa pamalo pake popumira ndi kukongola kwa dziko lake, iye anaweramutsa msana kuti anyamule katundu wake ndipo anasanduka wogwira ntchito ya ukapolo.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 49:15
10 Mawu Ofanana  

Isakara ndiye bulu wolimba, alinkugona pakati pa makola.


Dani adzaweruza anthu ake, monga limodzi la mafuko a Israele.


Ndipo kunali pakukhala mfumuyo m'nyumba mwake, atampumulitsa Yehova pa adani ake onse omzungulira,


Ndinamchotsera katundu paphewa pake, manja ake anamasuka ku chotengera.


Dzanja la akhama lidzalamulira; koma waulesi adzakhala ngati kapolo.


Pamenepo Asiriya adzagwa ndi lupanga losati la munthu; ndi lupanga losati la anthu lidzammaliza iye; ndipo iye adzathawa lupanga, ndi anyamata ake adzalamba.


Wobadwa ndi munthu iwe, Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni anachititsa ankhondo ake ntchito yaikulu yoponyana ndi Tiro; mitu yonse inachita dazi, ndi mapewa onse ananyuka; koma analibe kulandira mphotho ya ku Tiro, iye kapena ankhondo ake, pa ntchito anagwirayo;


Inde, amanga akatundu olemera ndi osautsa ponyamula, nawasenza pa mapewa a anthu; koma iwo eni okha safuna kuwasuntha amenewo ndi chala chao.


Koma kale dzina la Hebroni linali mzinda wa Araba, ndiye munthu wamkulu pakati pa Aanaki. Ndipo dziko linapumula nkhondo.


Pamenepo dziko linapumula zaka makumi anai; ndi Otiniyele mwana wa Kenazi anafa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa