Genesis 49:14 - Buku Lopatulika14 Isakara ndiye bulu wolimba, alinkugona pakati pa makola. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Isakara ndiye bulu wolimba, alinkugona pakati pa makola. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Isakara ali ngati bulu wamphamvu, amagona chotambasuka pakati pa makola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Isakara ali ngati bulu wamphamvu wogona pansi pakati pa makola. Onani mutuwo |