Genesis 48:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo anadalitsa Yosefe, nati, Mulungu, pamaso pake anayenda makolo anga Abrahamu ndi Isaki, Mulungu amene anandidyetsa ine nthawi zonse za moyo wanga kufikira lero, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo anadalitsa Yosefe, nati, Mulungu, pamaso pake anayenda makolo anga Abrahamu ndi Isaki, Mulungu amene anandidyetsa ine nthawi zonse za moyo wanga kufikira lero, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndipo adadalitsa Yosefe ndi mau akuti, “Mulungu amene makolo anga Abrahamu ndi Isaki adamtumikira, Mulungu amene wanditsogolera moyo wanga wonse mpaka lero lino, aŵadalitse anaŵa! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Kenaka anadalitsa Yosefe nati, “Mulungu amene makolo anga Abrahamu ndi Isake anamutumikira, Mulungu amene wakhala ali mʼbusa wanga moyo wanga wonse kufikira lero, Onani mutuwo |