Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 47:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Farao anati kwa Yakobo, Masiku a zaka za moyo wanu ndi angati?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Farao anati kwa Yakobo, Masiku a zaka za moyo wanu ndi angati?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Kenaka Farao adafunsa Yakobe kuti, “Muli ndi zaka zingati?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Atatero, Farao anafunsa Yakobo kuti, “Muli ndi zaka zingati?”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 47:8
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anamwalira, nafa mu ukalamba wake wabwino, nkhalamba ya zaka zambiri; natengedwa akhale ndi a mtundu wake.


Ndipo Yakobo anakhala m'dziko la Ejipito zaka khumi mphambu zisanu ndi ziwiri; ndipo masiku a Yakobo zaka za moyo wake zinali zaka zana limodzi mphambu makumi anai kudza zisanu ndi ziwiri.


Ndipo Yosefe analowa naye Yakobo atate wake, namuika iye pamaso pa Farao; ndipo Yakobo anamdalitsa Farao.


Ndipo Yakobo anati kwa Farao, Masiku a zaka za ulendo wanga ndi zaka zana limodzi kudza makumi atatu; masiku a zaka za moyo wanga ali owerengeka ndi oipa, sanafikire masiku a zaka za moyo wa makolo anga m'masiku a ulendo wao.


Koma Barizilai ananena ndi mfumu, Masiku a zaka za moyo wanga ndiwo angati, kuti ndiyenera kukwera ndi mfumu kunka ku Yerusalemu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa