Genesis 47:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Farao anati kwa Yakobo, Masiku a zaka za moyo wanu ndi angati? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Farao anati kwa Yakobo, Masiku a zaka za moyo wanu ndi angati? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Kenaka Farao adafunsa Yakobe kuti, “Muli ndi zaka zingati?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Atatero, Farao anafunsa Yakobo kuti, “Muli ndi zaka zingati?” Onani mutuwo |