Genesis 47:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Yosefe analowa naye Yakobo atate wake, namuika iye pamaso pa Farao; ndipo Yakobo anamdalitsa Farao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Yosefe analowa naye Yakobo atate wake, namuika iye pamaso pa Farao; ndipo Yakobo anamdalitsa Farao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Yosefe adatenga bambo wake Yakobe, napita naye kwa Farao. Ndipo Yakobe adadalitsa Faraoyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Kenaka Yosefe anapita ndi abambo ake kwa Farao kukawaonetsa, ndipo Yakobo anadalitsa Faraoyo. Onani mutuwo |