Genesis 47:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo Yakobo anakhala m'dziko la Ejipito zaka khumi mphambu zisanu ndi ziwiri; ndipo masiku a Yakobo zaka za moyo wake zinali zaka zana limodzi mphambu makumi anai kudza zisanu ndi ziwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo Yakobo anakhala m'dziko la Ejipito zaka khumi mphambu zisanu ndi ziwiri; ndipo masiku a Yakobo zaka za moyo wake zinali zaka zana limodzi mphambu makumi anai kudza zisanu ndi ziwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Yakobe adakhala ku Ejipito, zaka 17, choncho zaka za moyo wake zidakwanira 147. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Yakobo anakhala ku Igupto zaka 17 ndipo zaka za moyo wake zinali 147. Onani mutuwo |