Genesis 47:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo Israele anakhala m'dziko la Ejipito, m'dziko la Goseni; nakhala nazo zaozao m'menemo, nabalana nachuluka kwambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo Israele anakhala m'dziko la Ejipito, m'dziko la Goseni; nakhala nazo zaozao m'menemo, nabalana nachuluka kwambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Aisraele atakhazikika ku Ejipito, adalemera kwambiri, ndipo adaberekanso ana ambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Tsono Aisraeli anakhazikika mʼdziko la Igupto ku chigawo cha Goseni. Kumeneko anapeza chuma ndipo anaberekana nachuluka kwambiri. Onani mutuwo |