Genesis 47:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo munalibe chakudya m'dziko lonse; pakuti njala inalimba kwambiri; chifukwa chake dziko la Ejipito ndi dziko la Kanani linalefuka chifukwa cha njalayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo munalibe chakudya m'dziko lonse; pakuti njala inalimba kwambiri; chifukwa chake dziko la Ejipito ndi dziko la Kanani tinalefuka chifukwa cha njalayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Njala ija idakula kwambiri, kotero kuti panalibe chakudya pa dziko lonse lapansi, ndipo anthu a ku Ejipito ndi a ku Kanani komwe adafooka nayo njalayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Njala inakula kwambiri motero kuti chakudya chinasowa mʼdziko lonse. Anthu a ku Igupto ndi ku Kanaani analefuka nayo njalayo. Onani mutuwo |