Genesis 47:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Yosefe anachereza atate wake ndi abale ake, ndi mbumba yonse ya atate wake ndi chakudya monga mwa mabanja ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Yosefe anachereza atate wake ndi abale ake, ndi mbumba yonse ya atate wake ndi chakudya monga mwa mabanja ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Yosefe adapereka chakudya kwa bambo wake ndi kwa abale ake ndi kwa mbumba yonse, potsata kuchuluka kwa ana ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yosefe anaperekanso chakudya kwa abambo ake, kwa abale ake ndi kwa onse a mʼnyumba ya abambo ake monga mwa chiwerengero cha ana awo. Onani mutuwo |