Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 45:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo anakwera kutuluka mu Ejipito, nafika ku dziko la Kanani kwa Yakobo atate wao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo anakwera kutuluka m'Ejipito, nafika ku dziko la Kanani kwa Yakobo atate wao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Tsono iwo adachoka ku Ejipito, kubwerera ku Kanani kwa bambo wao Yakobe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Ndipo anachoka ku Igupto nafika kwa abambo awo Yakobo mʼdziko la Kanaani.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 45:25
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anadza kwa Yakobo atate wao ku dziko la Kanani, namfotokozera iye zonse zinaonekera kwa iwo;


Ndipo anamukitsa abale ake, ndipo anachoka; ndipo anati kwa iwo, Musakangane panjira.


Ndipo anamfotokozera iye kuti, Yosefe akali ndi moyo, ndipo alamulira m'dziko lonse la Ejipito. Pamenepo mtima wake unakomoka, pakuti sanawakhulupirire iwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa