Genesis 45:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo anamukitsa abale ake, ndipo anachoka; ndipo anati kwa iwo, Musakangane panjira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo anamukitsa abale ake, ndipo anachoka; ndipo anati kwa iwo, Musakangane panjira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Tsono adaŵauza abale akewo kuti azipita, ndipo ponyamukapo adanena kuti, “Musakangane pa njira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Kenaka anawalola abale ake aja kuti azipita, ndipo akunyamuka, iye anawawuza kuti, “Osakangana mʼnjira!” Onani mutuwo |