Genesis 45:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo ana a Israele anachita chotero: ndipo Yosefe anawapatsa iwo magaleta monga analamulira Farao, nawapatsa phoso la panjira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo ana a Israele anachita chotero: ndipo Yosefe anawapatsa iwo magaleta monga analamulira Farao, nawapatsa phoso la panjira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Tsono ana a Israele adachitadi zimenezo. Yosefe adaŵapatsa ngolo monga Farao adaalamulira, naŵapatsa phoso lapaulendo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Choncho ana a Israeli anachita zimenezo. Yosefe anawapatsa ngolo monga Farao analamulira, ndipo anawapatsanso chakudya cha paulendo wawo. Onani mutuwo |