Genesis 45:20 - Buku Lopatulika20 Musasamalire chuma chanu; popeza zabwino za dziko lonse la Ejipito ndi zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Musasamalire chuma chanu; popeza zabwino za dziko lonse la Ejipito ndi zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Asakade nkhaŵa kuti asiya katundu wao kumeneko, chifukwa dziko lokoma lachonde la ku Ejipito kuno lidzakhala lao.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Musadandaule zosiya katundu komweko chifukwa dziko lachonde la kuno ku Igupto lidzakhala lanu.’ ” Onani mutuwo |