Genesis 45:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo Farao anati kwa Yosefe, Nena ndi abale ako, Chitani ichi; senzetsani nyama zanu, ndi kupita kunka ku dziko la Kanani; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo Farao anati kwa Yosefe, Nena ndi abale ako, Chitani ichi; senzetsani nyama zanu, ndi kupita kunka ku dziko la Kanani; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ndipo Farao adauza Yosefe kuti, “Uŵauze abale ako kuti asenzetse nyama zao katundu, ndipo abwerere ku Kanani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Farao anati kwa Yosefe, “Uwawuze abale ako kuti, ‘Senzetsani nyama zanu katundu ndi kubwerera ku dziko la Kanaani. Onani mutuwo |