Genesis 45:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo mbiri yake inamveka m'nyumba ya Farao, kuti abale ake a Yosefe afika; ndipo inamkomera Farao, ndi anyamata ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo mbiri yake inamveka m'nyumba ya Farao, kuti abale ake a Yosefe afika; ndipo inamkomera Farao, ndi anyamata ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Zitamveka kunyumba kwa Farao kuti abale a Yosefe abwera, Faraoyo ndi antchito ake onse adakondwa kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Akunyumba kwa Farao atamva kuti abale ake a Yosefe abwera, Farao pamodzi ndi nduna zake zonse anakondwera. Onani mutuwo |