Genesis 45:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Yosefe sanakhoze kudziletsa pamaso pa onse amene anaima naye: nati, Tulutsa anthu onse pamaso panga. Ndipo panalibe munthu pamodzi ndi iye pamene Yosefe anadziululira yekha kwa abale ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Yosefe sanakhoze kudziletsa pamaso pa onse amene anaima naye: nati, Tulutsa anthu onse pamaso panga. Ndipo panalibe munthu pamodzi ndi iye pamene Yosefe anadziululira yekha kwa abale ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pamenepo Yosefe sadathenso kudzigwira pamaso pa onse omtumikira aja. Adanena mokweza mau kuti, “Onse atuluke muno.” Motero panalibe ndi mmodzi yemwe wotsalira pamene Yosefe ankadziwulula kwa abale ake aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsono Yosefe sanathenso kuwugwira mtima kuti asalire pamaso pa antchito ake ndipo anafuwula kuti, “Aliyense achoke pamaso panga!” Motero panalibe wina aliyense pamene Yosefe anadziwulula kwa abale ake. Onani mutuwo |