Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 44:34 - Buku Lopatulika

34 Pakuti ndidzakwera bwanji kwa atate wanga, mnyamatayo akapanda kukhala ndi ine? Ndingaone choipa chidzagwera atate wanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Pakuti ndidzakwera bwanji kwa atate wanga, mnyamatayo akapanda kukhala ndi ine? Ndingaone choipa chidzagwera atate wanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Ine ndingathe bwanji kupita kwa bambo wanga popanda mnyamatayu kupita nane? Ine ndekha sindingathe kupirira kuti ndiwone tsoka lotere likugwera bambo wanga.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Ndingabwerere bwanji kwa abambo anga ngati sindingapite ndi mnyamatayu? Ayi! Sindifuna kukaona tsoka limene lingakagwere abambo anga.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 44:34
10 Mawu Ofanana  

Tsopanotu, mtumiki wanu akhale kapolo wa mbuyanga m'malo mwa mnyamata; mnyamatayo akwere pamodzi ndi abale ake.


Ndipo Yosefe sanakhoze kudziletsa pamaso pa onse amene anaima naye: nati, Tulutsa anthu onse pamaso panga. Ndipo panalibe munthu pamodzi ndi iye pamene Yosefe anadziululira yekha kwa abale ake.


Taona, ndidzakusonkhanitsa kumakolo ako, nudzaikidwa kumanda kwako mumtendere, ndi maso ako sadzapenya zoipa zonse ndidzafikitsira malo ano ndi okhala m'mwemo. Ndipo anambwezera mfumu mau.


pakuti ndidzapirira bwanji pakuchiona choipa chilikudzera a mtundu wanga, kapena ndidzapirira bwanji pakuchiona chionongeko cha fuko langa?


Ngati ndakondwera nalo tsoka la wondida, kapena kudzitukula pompeza choipa;


Zingwe za imfa zinandizinga, ndi zowawa za manda zinandigwira: ndinapeza nsautso ndi chisoni.


Kusautsika ndi kupsinjika kwandigwera; koma malamulo anu ndiwo ondikondweretsa ine.


Ndipo Mose anafotokozera mpongozi wake zonse Yehova adazichitira Farao ndi Aejipito chifukwa cha Israele; ndi mavuto onse anakomana nao panjira, ndi kuti Yehova adawalanditsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa