Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 44:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo anapeza iwo, nanena nao mau omwewo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo anapeza iwo, nanena nao mau omwewo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Wantchito uja ataŵapeza, adanena mau omwe adaamuuza aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Wantchito uja atawapeza ananena mawu anawuzidwa aja.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 44:6
3 Mawu Ofanana  

Kodi si ndicho chomwera nacho mbuyanga, naombeza ula nacho? Mwachitira choipa pakutero.


Nati kwa iye, Bwanji mbuyanga anena mau otere? Ngati nkutheka kuti akapolo anu achite chotero?


Pakuti, taonani, ichi chomwe, chakuti mudamvetsedwa chisoni cha kwa Mulungu, khama lalikulu lanji chidalichita mwa inu, komanso chodzikonza, komanso mkwiyo, komanso mantha, komanso kukhumbitsa komanso changu, komanso kubwezera chilango! M'zonse munadzitsimikizira nokha kuti muli oyera mtima m'menemo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa