Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 44:13 - Buku Lopatulika

13 ndipo anang'amba zovala zao, nasenzetsa yense bulu wake, nabwera kumzinda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 ndipo anang'amba zovala zao, nasenzetsa yense bulu wake, nabwera kumudzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Apo onsewo adang'amba zovala zao ndi chisoni. Adasenzetsanso abulu katundu wao uja, nabwerera kumzinda konkuja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Apo onse anangʼamba zovala zawo ndi chisoni. Ndipo anasenzetsa abulu katundu wawo nabwerera ku mzinda konkuja.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 44:13
7 Mawu Ofanana  

Atatuluka m'mzinda asanamuke patali, Yosefe anati kwa tsanyumba wake, Tanyamuka, talondola anthu aja, ukawapeza unene nao, Chifukwa chanji mwabwezera zoipa m'malo mwa zabwino?


Pomwepo Davide anagwira zovala zake nazing'amba; nateronso anthu onse okhala naye.


pa tsiku lachitatu, onani, munthu anatuluka ku zithando za Saulo, ali ndi zovala zake zong'ambika, ndi dothi pamutu pake; ndipo kunatero kuti iye, pofika kwa Davide, anagwa pansi namgwadira.


Ndipo Tamara anathira phulusa pamutu pake, nang'amba chovala cha mawangamawanga chimene analikuvala, nagwira dzanja lake pamutu pake, namuka nayenda, nalira komveka.


napenya, ndipo taonani, mfumu ili chilili pachiundo, monga ankachita, ndi atsogoleri ndi amalipenga pali mfumu; nakondwerera anthu onse a m'dziko, naomba malipenga. Pamenepo Ataliya anang'amba zovala zake, nafuula Chiwembu, Chiwembu.


Ndipo Yoswa mwana wa Nuni, ndi Kalebe mwana wa Yefune, ndiwo a iwo aja adazonda dzikolo, anang'amba zovala zao;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa