Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 44:14 - Buku Lopatulika

14 Yudanso ndi abale ake anadza kunyumba ya Yosefe; ndipo iye akali pamenepo; ndipo anagwa pansi patsogolo pake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Yudanso ndi abale ake anadza kunyumba ya Yosefe; ndipo iye akali pamenepo; ndipo anagwa pansi patsogolo pake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Yuda ndi abale ake atafika kunyumba kwa Yosefe, adampeza akadali momwemo ndipo onsewo adaŵerama pamaso pake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Pamene Yuda ndi abale ake ankafika ku nyumba kwa Yosefe nʼkuti Yosefe akanali komweko. Ndipo anadzigwetsa pansi pamaso pake.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 44:14
5 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Yosefe anaona Benjamini pamodzi nao, anati kwa tsanyumba wake, Lowa nao anthuwo m'nyumba, kaphere iwo, kakonzere, chifukwa anthuwo adzadya ndi ine usana uno.


Ndipo anakonzeratu mphatso asanafike Yosefe usana; chifukwa anamva kuti adzadya chakudya pamenepo.


Ndiponso abale ake anamuka namgwadira pamaso pake; nati, Taonani, ife ndife akapolo anu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa