Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 44:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo iye anafunafuna kuyambira pa wamkulu naleka pa wamng'ono nachipeza chikho m'thumba la Benjamini:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo iye anafunafuna kuyambira pa wamkulu naleka pa wamng'ono nachipeza chikho m'thumba la Benjamini:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Wantchito wa Yosefe uja adafunafuna mosamala kwambiri kuyambira pa wamkulu mpaka pa wamng'ono, ndipo chikhocho adachipeza m'thumba la Benjamini.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Kenaka anayamba kufufuza, kuyambira pa wamkulu mpaka pa wamngʼono. Ndipo chikhocho chinapezeka mʼthumba mwa Benjamini.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 44:12
6 Mawu Ofanana  

Mulungu Wamphamvuyonse adzakupatsani inu chifundo pamaso pa munthu uja, kuti akumasulireni inu mbale wanu wina ndi Benjamini. Ndipo ine, ngati ndikhala wopanda ana, ndikhalatu.


Ndipo anakhala pamaso pake, woyamba monga ukulu wake, ndi wamng'ono monga ung'ono wake; ndipo anazizwa wina ndi wina.


Ndipo anafulumira natsitsa pansi yense thumba lake, namasula yense thumba lake.


Nuike chikho changa, chikho chasiliva chija, kukamwa kwa thumba la wamng'ono, pamodzi ndi ndalama za tirigu zake. Ndipo iye anachita monga mau ananena Yosefe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa