Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 44:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo anafulumira natsitsa pansi yense thumba lake, namasula yense thumba lake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo anafulumira natsitsa pansi yense thumba lake, namasula yense thumba lake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Motero onsewo adatsitsa msanga matumba ao, aliyense nkumasula thumba lake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Tsono onse anafulumira kutsitsa pansi aliyense thumba lake ndi kulitsekula.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 44:11
3 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene wina wa iwo anamasula thumba lake kuti adyetse bulu wake pachigono, anapeza ndalama zake; taonani, zinali kukamwa kwa thumba lake.


Ndipo iye anati, Tsononso chikhale monga mwa mau anu: iye amene ampeza nacho adzakhala kapolo wanga; ndipo inu mudzakhala opanda chifukwa.


Ndipo iye anafunafuna kuyambira pa wamkulu naleka pa wamng'ono nachipeza chikho m'thumba la Benjamini:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa