Genesis 43:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo anafunsa iwo za ubwino wao, nati, Kodi atate wanu ali ndi moyo? Wokalamba uja amene munanena uja: kodi alipo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo anafunsa iwo za ubwino wao, nati, Kodi atate wanu ali ndi moyo? Wokalamba uja amene munanena uja: kodi alipo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Iye adaŵafunsa m'mene aliri, naŵafunsanso kuti, “Kodi bambo wanu wokalamba uja munkandiwuzayu ali bwanji? Kodi akali moyo?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Yosefe anawafunsa za moyo wawo kenaka anati, “Kodi abambo anu wokalamba amene munkandiwuza aja ali bwanji? Ali ndi moyobe?” Onani mutuwo |