Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 43:28 - Buku Lopatulika

28 Ndipo iwo anati, Kapolo wanu atate wathu ali bwino, alipo. Ndipo anawerama, namgwadira iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ndipo iwo anati, Kapolo wanu atate wathu ali bwino, alipo. Ndipo anawerama, namgwadira iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Iwowo adayankha kuti, “Mtumiki wanu akali moyo, ndipo ali bwino.” Tsono onsewo adamgwadiranso namuŵeramira pomwepo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Iwo anayankha kuti, “Mtumiki wanu abambo athu akanali ndi moyo ndipo ali bwino.” Ndipo anamugwadira namuweramira pansi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 43:28
8 Mawu Ofanana  

pakuti taonani, ndinalinkumanga mitolo m'munda, ndipo taonani, mtolo wanga unauka nuima chilili! Ndipo taonani, mitolo yanu inadza niuzinga kwete, niuweramira mtolo wanga.


Pamene Yosefe anadza kunyumba kwake, analowa nazo m'nyumba mphatso zinali m'manja mwao, namweramira iye pansi.


pa tsiku lachitatu, onani, munthu anatuluka ku zithando za Saulo, ali ndi zovala zake zong'ambika, ndi dothi pamutu pake; ndipo kunatero kuti iye, pofika kwa Davide, anagwa pansi namgwadira.


Ndipo pamene mkazi wa ku Tekowayo anati alankhule ndi mfumuyo, anagwa nkhope yake pansi, namlambira, nati, Ndithandizeni mfumu.


Ndipo Bateseba anawerama nalambira mfumu, ndi mfumu niti, Ufunanji?


Atamwalira Yehoyada tsono, akalonga a Yuda anadza, nalambira mfumu. Ndipo mfumu inawamvera.


Ndipo Mose anatuluka kukakomana ndi mpongozi wake, nawerama, nampsompsona; nafunsana ali bwanji, nalowa m'hema.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa