Genesis 43:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo iwo anati, Kapolo wanu atate wathu ali bwino, alipo. Ndipo anawerama, namgwadira iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo iwo anati, Kapolo wanu atate wathu ali bwino, alipo. Ndipo anawerama, namgwadira iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Iwowo adayankha kuti, “Mtumiki wanu akali moyo, ndipo ali bwino.” Tsono onsewo adamgwadiranso namuŵeramira pomwepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Iwo anayankha kuti, “Mtumiki wanu abambo athu akanali ndi moyo ndipo ali bwino.” Ndipo anamugwadira namuweramira pansi. Onani mutuwo |