Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 43:26 - Buku Lopatulika

26 Pamene Yosefe anadza kunyumba kwake, analowa nazo m'nyumba mphatso zinali m'manja mwao, namweramira iye pansi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Pamene Yosefe anadza kunyumba kwake, analowa nazo m'nyumba mphatso zinali m'manja mwao, namweramira iye pansi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Yosefe atabwera, abale akewo adapereka mphatso zija kwa iye, ndipo adamuweramira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Yosefe atafika ku nyumbako, iwo anapereka mphatso zija namuweramira pansi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 43:26
11 Mawu Ofanana  

Anthu akutumikire iwe, mitundu ikuweramire iwe; uchite ufumu pa abale ako, ana a amai ako akuweramire iwe. Wotemberereka aliyense akutemberera iwe, wodalitsika aliyense akudalitsa iwe.


Ndipo iye mwini anatsogolera patsogolo pao, nawerama pansi kasanu ndi kawiri mpaka anayandikira mkulu wake.


Ndipo Yosefe anali wolamulira dziko; ndiye amene anagulitsa kwa anthu onse a m'dziko; ndipo anafika abale ake a Yosefe, namweramira pansi, nkhope zao pansi.


Ndipo Israele atate wao anati kwa iwo, Ngati chomwecho tsopano chitani ichi: tengani zipatso za m'dziko muno m'zotengera zanu, mumtengere munthu uja mphatso, mafuta amankhwala pang'ono, ndi uchi pang'ono, zonunkhira ndi mure, ndi mfula, ndi katungurume;


Ndipo iwo anati, Kapolo wanu atate wathu ali bwino, alipo. Ndipo anawerama, namgwadira iye.


Okhala m'chipululu adzagwadira pamaso pake; ndi adani ake adzaluma nthaka.


Ndipo Mose anatuluka kukakomana ndi mpongozi wake, nawerama, nampsompsona; nafunsana ali bwanji, nalowa m'hema.


Pakuti kwalembedwa, Pali moyo wanga, ati Ambuye, mabondo onse adzagwadira Ine, ndipo malilime onse adzavomereza Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa