Genesis 43:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo munthuyo analowetsa anthu m'nyumba ya Yosefe, nawapatsa iwo madzi, natsuka mapazi ao, napatsa abulu ao chakudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo munthuyo analowetsa anthu m'nyumba ya Yosefe, nawapatsa iwo madzi, natsuka mapazi ao, napatsa abulu ao chakudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Wantchitoyo atabwera nawo abalewo m'nyumba mwa Yosefe, adaŵapatsa madzi kuti asambe mapazi ao, ndipo abulu ao aja adaŵadyetsanso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Wantchito uja anawalowetsa anthuwo mʼnyumba ya Yosefe, nawapatsa madzi kuti asambe mapazi awo. Anadyetsanso abulu awo. Onani mutuwo |