Genesis 43:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo iye anati, Mtendere ukhale ndi inu, musaope; Mulungu wanu ndi Mulungu wa atate wanu anakupatsani inu chuma m'matumba anu; ine ndinali nazo ndalama zanu. Pamenepo anawatulutsira Simeoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo iye anati, Mtendere ukhale ndi inu, musaope; Mulungu wanu ndi Mulungu wa atate wanu anakupatsani inu chuma m'matumba anu; ine ndinali nazo ndalama zanu. Pamenepo anawatulutsira Simeoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Wantchito uja adati, “Musade nkhaŵa, mitima yanu ikhale pansi. Mulungu wanu, Mulungu wa atate anu, ndiye amene adakuikirani ndalama zanu m'matumbamo. Ndalama zanu zoyamba zija ndidalandira.” Atatero, adaŵatulutsira Simeoni uja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Koma iye anati, “Mitima yanu ikhale pansi ndipo musachite mantha. Mulungu wanu, Mulungu wa abambo anu, anakuyikirani chumacho mʼmatumba anu. Ine ndinalandira ndalama zanu.” Ndipo anakawatulutsira Simeoni. Onani mutuwo |