Genesis 43:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo anayandikira kwa tsanyumba wa Yosefe, ndipo ananena ndi iye pa khomo la nyumba, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo anayandikira kwa tsanyumba wa Yosefe, ndipo ananena ndi iye pa khomo la nyumba, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Motero asanaloŵe m'nyumbamo adafika kwa wantchito wa Yosefe woyang'anira nyumba uja, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Choncho atafika pa khomo la nyumba ya Yosefe anamuyandikira wantchito wa Yosefe nayankhula naye kuti, Onani mutuwo |