Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 43:17 - Buku Lopatulika

17 Munthuyo anachita monga anamuuza Yosefe, ndipo munthuyo analowa nao anthuwo m'nyumba ya Yosefe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Munthuyo anachita monga anamuuza Yosefe, ndipo munthuyo analowa nao anthuwo m'nyumba ya Yosefe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Wantchitoyo adachita monga momwe Yosefe adamuuzira, napita nawo abale aja kunyumba kwa Yosefe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Wantchitoyo anachita monga momwe Yosefe ananenera, ndipo anawatengera abale aja ku nyumba kwa Yosefe.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 43:17
2 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Yosefe anaona Benjamini pamodzi nao, anati kwa tsanyumba wake, Lowa nao anthuwo m'nyumba, kaphere iwo, kakonzere, chifukwa anthuwo adzadya ndi ine usana uno.


Anthuwo ndipo anaopa, chifukwa analowezedwa m'nyumba ya Yosefe; nati, Chifukwa cha ndalama zija zinabwezedwa m'matumba athu nthawi yoyamba ija, ife tilowezedwa, kuti aone chifukwa ndi ife, atigwere ife, atiyese ife akapolo, ndi abulu athu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa