Genesis 42:32 - Buku Lopatulika32 tili abale khumi ndi awiri, ana a atate wathu; wina palibe, ndipo lero wamng'ono ali ndi atate wathu m'dziko la Kanani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 tili abale khumi ndi awiri, ana a atate wathu; wina palibe, ndipo lero wamng'ono ali ndi atate wathu m'dziko la Kanani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Ife tonse tinalipo ana aamuna khumi ndi aŵiri, koma mmodzi adamwalira, ndipo wamng'ono ali ndi bambo wathu ku Kanani.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Ife tonse tinalipo ana aamuna khumi ndi awiri, abambo mmodzi. Mmodzi anamwalira, ndipo wamngʼono ali ndi abambo athu ku Kanaani.’ ” Onani mutuwo |