Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 42:31 - Buku Lopatulika

31 Koma ife tinati kwa iye, Tili anthu oona; sitili ozonda;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Koma ife tinati kwa iye, Tili anthu oona; sitili ozonda;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Ife tidamuuza munthuyo kuti, ‘Ndife anthu okhulupirika, osati azondi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Koma tinamuwuza kuti, ‘Ndife anthu woona mtima osati akazitape.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 42:31
2 Mawu Ofanana  

Tonse tili ana aamuna a munthu mmodzi; tili oona, akapolo anu, sitili ozonda.


tili abale khumi ndi awiri, ana a atate wathu; wina palibe, ndipo lero wamng'ono ali ndi atate wathu m'dziko la Kanani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa